Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 11:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Ine ndine Yehova Mulungu wanu.+ Mudzipatule ndi kukhala oyera,+ chifukwa ine ndine woyera.+ Choncho musamadzidetse ndi chamoyo chilichonse choyenda padziko lapansi.

  • Levitiko 19:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Uza gulu lonse la Aisiraeli kuti, ‘Mukhale oyera, chifukwa ine Yehova Mulungu wanu ndine woyera.+

  • Levitiko 20:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Choncho mudzipatule ndipo mukhale oyera,+ chifukwa ine ndine Yehova Mulungu wanu.

  • Levitiko 20:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Mukhale oyera kwa ine, chifukwa ine Yehova ndine woyera.+ Ine ndikukusiyanitsani ndi anthu a mitundu ina kuti mukhale anthu anga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena