Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 7:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Kenako iye anapanga thanki yosungira madzi.*+ Thankiyo inali yozungulira ndipo inali mikono 10 kuchokera mbali ina kufika ina, kuyeza modutsa pakati. Thankiyo inali yaitali mikono 5 ndipo kuzungulira thanki yonseyo inali mikono 30.+

  • Chivumbulutso 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Patsogolo pa mpando wachifumuwo, panali chinachake chooneka ngati nyanja ya galasi+ komanso ngati mwala wa kulusitalo.

      Pakati pa mpando wachifumuwo ndiponso kuzungulira mpandowo, panali angelo 4+ amene anali ndi maso ambirimbiri, kutsogolo ndi kumbuyo komwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena