Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g91 9/8 tsamba 32
  • Pamene Agogo Ake Anamwalira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pamene Agogo Ake Anamwalira
  • Galamukani!—1991
Galamukani!—1991
g91 9/8 tsamba 32

Pamene Agogo Ake Anamwalira

Nakubala wa ku Virginia Beach, Virginia, U.S.A., analemba kuti: “Mwezi watha atate wanga anamwalira. Iwo ndi mwana wanga wamwamuna wamng’ono kwambiri ankakondana kwambiri, mosasamala kanthu za mtunda womwe unali pakati pawo. Pamene ndinamudziŵitsa kuti agogo ake amwalira, anayamba kulira momvetsa chisoni.

“Ndinafunafuna mofulumira trakiti yakuti Kodi Pali Chiyembekezo Chotani Kaamba ka Okondedwa Akufa? Mwamsanga nditaipeza, pamene nkhope yake inali idakali ndi misozi, ndinayamba kumuŵerengera. Pamene ndinamaliza, iye anatontholako. Ndikuthokozani kaamba ka chidziŵitso chamtengo wake choterocho, chomwe chinali chothandiza kwambiri panthaŵi yowawitsa imeneyi.”

Mukhoza kulandira trakiti yotonthoza imeneyi, limodzi ndi ena, mwakungodzaza ndi kutumiza kapepala kotsatiraka.

Ndingakonde kulandira trakiti uakuti Kodi Pali Chiyembekezo Chotani Kaamba ka Okondedwa Akufa? limodzi ndi matrakiti ena. (Kunja kwa Zambia, lemberani ku nthambi ya Watch Tower yakwanuko kaamba ka chidziŵitso. Onani tsamba 5.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena