Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g92 11/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1992
  • Timitu
  • Kodi Zosangulutsa Zimayambukira Motani Moyo Wanu? 3-10
  • Kupulumutsidwa ku Imfa ndi Chithandizo Chamankhwala Popanda Mwazi 22
Galamukani!—1992
g92 11/8 tsamba 2

Tsamba 2

Kodi Zosangulutsa Zimayambukira Motani Moyo Wanu? 3-10

Kusanguluka ndiko chofunika chabwino cha anthu. Koma moyo wa zosangulutsa ulinso malonda aakulu. Ndipo monga momwedi chikomekome chankhuyu mkati muli nyerere, choteronso sizosangulutsa zonse zimene ziridi zabwino. Kodi ndizosangulutsa zotani zimene mumasankha? Kodi chosankha chanu chimanenanji ponena za inu?

Kupulumutsidwa ku Imfa ndi Chithandizo Chamankhwala Popanda Mwazi 22

Ambiri lerolino amapempha mankhwala opanda mwazi mumkhalidwe wamwadzidzidzi wazamankhwala. Ŵerengani mmene wodwala wina analandirira mankhwala opatsa moyo oterowo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena