Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • be tsamba 2-3
  • Zam’katimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zam’katimu
  • Pindulani ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu
  • Timitu
  • Mmene Mungapitire Patsogolo
Pindulani ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu
be tsamba 2-3

Zam’katimu

Tsamba

5 Takulandirani ku Sukulu ya Utumiki wa Mulungu

9 Kondwerani ndi Mawu a Mulungu

13 “Yang’anirani Mamvedwe Anu”

17 Mukhoza Kunola Luso Lanu Lokumbukira Zinthu

21 Chitani Khama pa Kuŵerenga

27 Kuphunzira Kumapindulitsa

33 Mmene Mungafufuzire

39 Kukonza Autilaini

43 Kukonzekera Nkhani ya Wophunzira mu Sukulu

47 Kukonzekera Nkhani Zokambira Mpingo

52 Kukonzekera Nkhani za Onse

56 Kulitsani Luso la Kuphunzitsa

62 Mmene Mungakulitsire Luso la Kucheza ndi Anthu

66 Dziŵani Mayankhidwe Oyenera

71 Kukambirana M’makalata

74 Khalani Womapitabe Patsogolo

78 Pulogalamu Yophunzitsa Luso la Kulankhula ndi Kuphunzitsa

79 Fomu Yolangizira

82 Gwiritsani Ntchito Mitundu Yosiyanasiyana ya Makambirano

Mmene Mungapitire Patsogolo

Tsamba Phunziro

83 1 Kuŵerenga Molondola

86 2 Kulankhula Momveka Bwino

89 3 Kutchula Mawu Molondola

93 4 Kulankhula Mosadodoma

97 5 Kupuma Koyenerera

101 6 Kutsindika Ganizo Moyenerera

105 7 Kutsindika Malingaliro Ofunika Kwambiri

107 8 Mphamvu ya Mawu Yoyenerera

111 9 Kusinthasintha Mawu

115 10 Kulankhula Mwaumoyo

118 11 Mzimu Waubwenzi ndi Mmene Mukumvera

121 12 Manja ndi Nkhope Polankhula

124 13 Kuyang’ana Omvera

128 14 Kulankhula Mwachibadwa

131 15 Kuoneka Bwino

135 16 Kudekha

139 17 Kugwiritsa Ntchito Maikolofoni

143 18 Kugwiritsa Ntchito Baibulo Popereka Mayankho

145 19 Kulimbikitsa Omvera Kuŵerenga Baibulo

147 20 Kutchula Malemba Moyenerera

150 21 Kutsindika Malemba Moyenerera

153 22 Kugwiritsa Ntchito Malemba Moyenerera

157 23 Kumveketsa Phindu la Nkhani Yanu

160 24 Kusankha Bwino Mawu

166 25 Kugwiritsa Ntchito Autilaini

170 26 Kukamba Nkhani M’njira Yotsatirika

174 27 Kulankhula Kuchokera mu Mtima

179 28 Kukamba Nkhani Mmene Mumalankhulira ndi Anthu

181 29 Kamvekedwe Kabwino ka Mawu

186 30 Kusonyeza Chidwi mwa Munthu Winayo

190 31 Kulemekeza Ena

194 32 Kulankhula Motsimikiza

197 33 Khalani Wosamala Komanso Wolimba

202 34 Khalani Wolimbikitsa

206 35 Kubwereza Komveketsa Mfundo

209 36 Kutambasula Mutu wa Nkhani

212 37 Kuunika Mfundo Zazikulu

215 38 Mawu Oyamba Okopa Chidwi

220 39 Mawu Omaliza Ogwira Mtima

223 40 Kunena Zoona Zokhazokha

226 41 Lankhulani Zomveka Bwino kwa Ena

230 42 Nkhani Yophunzitsadi Kanthu Omvera

234 43 Kukamba Mfundo za M’nkhani Imene Mwapatsidwa

236 44 Kugwiritsa Ntchito Mafunso Mwaluso

240 45 Mafanizo ndi Zitsanzo Zophunzitsadi

244 46 Mafanizo a Zinthu Zodziŵika Bwino

247 47 Kugwiritsa Ntchito Mwaluso Zinthu Zooneka Pophunzitsa

251 48 Njira Yokambirana

255 49 Kupereka Zifukwa Zomveka

258 50 Yesetsani Kuwafika Pamtima Anthu

263 51 Kusunga Nthaŵi ndi Kuigaŵa Bwino

265 52 Kulimbikitsa Ena Mogwira Mtima Kuti Achitepo Kanthu

268 53 Kulimbikitsa Omvera ndi Kuwatsitsimutsa

272 Uthenga Umene Tiyenera Kulengeza

282 Malangizo kwa Oyang’anira Sukulu

286 Mlozera Nkhani

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena