Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 12
  • Yehova Mulungu Wamkulu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Mulungu Wamkulu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova, Mulungu Wamkulu
    Imbirani Yehova
  • M’patseni Yehova Ulemerero
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 12

NYIMBO 12

Yehova Mulungu Wamkulu

Losindikizidwa

(Ekisodo 34:​6, 7)

  1. 1. Inu Yehova M’lungu Wamkulu,

    Wabwino m’zinthu zonse,

    Tizikutamandani.

    Muli ndi mphamvu, chikondi, nzeru.

    Mulungu wathu ndinu.

  2. 2. Tikumaona chifundo chanu.

    Ngakhale ndife fumbi

    Tikapempha mumamva.

    Mumatidyetsa, kutiphunzitsa,

    Mumatithandizadi.

  3. 3. Tikutamanda inu Yehova.

    Tikukuimbirani

    Mosangalala ndithu.

    Muyeneradi kutamandidwa

    Kuchokera mumtima.

(Onaninso Deut. 32:4; Miy. 16:12; Mat. 6:10; Chiv. 4:11.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena