Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 15
  • Tamandani Mwana Woyamba Kubadwa wa Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tamandani Mwana Woyamba Kubadwa wa Yehova
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tamandani Mfumu Yatsopano Yolamulira Dziko Lapansi
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 15

NYIMBO 15

Tamandani Mwana Woyamba Kubadwa wa Yehova

Losindikizidwa

(Aheberi 1:6)

  1. 1. Tamandani Yesu

    Mfumu yodzozedwayo,

    Yokonda choonadi 

    Komanso chilungamo. 

    Atavala ulemu 

    Ndi ulemerero, 

    Adzayeretsa dzina

    La Yehova M’lungu.

    (KOLASI)

    Tamandani Yesu 

    Wodzozedwa wa M’lungu.

    Wakhala pa Ziyoni 

    Mongadi Mfumu yathu.

  2. 2. Tamandani Yesu

    Yemwe anatifera. 

    Anapereka dipo, 

    Timakhululukidwa.

    Mkwatibwi wake pano 

    Akudikirira 

    Kuti alamulire 

    Limodzi ndi Yesu. 

    (KOLASI)

    Tamandani Yesu 

    Wodzozedwa wa M’lungu.

    Wakhala pa Ziyoni 

    Mongadi Mfumu yathu.

(Onaninso Sal. 2:6; 45:​3, 4; Chiv. 19:8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena