Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w03 12/15 tsamba 31
  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 2003

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 2003
  • Nsanja ya Olonda—2003
  • Timitu
  • BAIBULO
  • MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA
  • MBIRI YA MOYO WANGA
  • MBONI ZA YEHOVA
  • MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU
  • NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • YEHOVA
  • YESU KRISTU
Nsanja ya Olonda—2003
w03 12/15 tsamba 31

Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 2003

Zosonyeza deti la kope lopezekamo nkhaniyo

BAIBULO

Anthu Wamba Anamasulira (Chitahiti), 7/1

Kulunjika Nawo Bwino Mawu a Choonadi, 1/1

MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA

Chifukwa chake manambala a mavesi m’buku la Masalmo amasiyana, 4/1

Chifuniro cha Mulungu chnachitika kale kumwamba? (Mat. 6:10), 12/15

Ezekieli anakhala wosalankhula? (Ezek. 24:27; 33:22), 12/1

Kubatizidwa chifukwa cha akufa (1 Akor. 15:29, KJ), 10/1

Kulumbira pofuna kunena zoona zokhazokha m’khoti? 1/15

Kumva mawu koma osaona amene akulankhula, ndiye kuti ziwanda n’zimene zikum’vutitsa, 5/1

“Magawo aŵiri” a mzimu wa Eliya (2 Maf. 2:9), 11/1

Mfundo ya mitala inasintha? 8/1

Miyala ya miyezi yobadwira, 11/15

“Mmodzi wa ife” (Gen. 3:22), 10/15

‘Moyo mwa Iye yekha’ (Yoh. 5:26; 6:53), 9/15

Mphatso za ukwati, 9/1

N’chifukwa chiyani munthu ayenera kufuula ngati wina akufuna kumugwirira? 2/1

N’kulakwa kupha galu kapena mphaka? 6/1

“Nthaŵi zonse” (1 Akor. 11:25, 26), 1/1

‘Onani Mlangizi,’ ‘Imvani mawu kumbuyo’ (Yes. 30:20, 21), 2/15

Pamene wodzozedwa yemwe akudwala sangathe kupezekapo pa Chikumbutso, 3/15

Satana ‘ali nayo mphamvu ya imfa’? (Aheb. 2:14), 7/1

Satana amatha kudziŵa zimene munthu akuganiza? 6/15

Ubatizo wa mu 33 C.E. unasonyeza kudzipatulira? 5/15

MBIRI YA MOYO WANGA

Anali Wokoma Mtima (M. Henschel), 8/15

Chimwemwe Chosayerekezeka! (R. Wallwork), 6/1

Kakalata Kamene Kanasintha Moyo Wanga (I. Hochstenbach), 1/1

Kufunafuna Ufumu Choyamba Ndiwo Moyo Wabwino ndi Wosangalatsa (J. Sunal), 3/1

Kuphunzitsidwa ndi Yehova Kuyambira pa Ubwana Wanga (R. Abrahamson), 11/1

Kutumikira Ena Kumachepetsa Mavuto (J. Arias), 7/1

Kuyesedwa mu Ng’anjo Yamoto (P. Yannouris), 2/1

“Ndidzabwezera Yehova Chiyani?” (M. Kerasinis), 12/1

Wodala Munthu Amene Mulungu Wake ndi Yehova (T. Didur), 8/1

Yehova Amakokera Anthu Odzichepetsa (A. Koshino), 10/1

Yehova Amatisamalira Nthaŵi Zonse (E. Mzanga), 9/1

Zimene Ndachitako pa Ntchito ya Padziko Lonse Yophunzitsa Baibulo (R. Nisbet), 4/1

MBONI ZA YEHOVA

Asanaphunzire ndi Ataphunzira, 1/15, 3/15, 5/15, 7/15, 9/15, 11/15

Atumiki a M’mayiko Ena (Dziko la Mexico), 5/1

Chizunzo, 3/1

Dziko la Brazil (gawo la osamva), 2/1

Dziko la Czech Republic, 8/1

Dziko la France, 12/1

Dziko la Poland, 10/1

Dziko la Ukraine, 10/1

Kalendala, 11/15

Khoti Lalikulu Lagamula Kuti Kulambira Koona Kupitirire (Dziko la Armenia), 4/1

Kukumbukira Amene Anaphedwa (Dziko la Hungary), 1/15

Kulalikira Kumakhaladi Kosaiŵalika (Dziko la Mexico), 4/15

Kulambira Koona Kugwirizanitsa Banja, 8/15

Kupindula Chifukwa cha Khama, 1/1

Kuthandizidwa Poonabe Magazi Kukhala Opatulika (Dziko la Philippines), 5/1

‘Linakwaniritsa Chimene Ndinkafuna Kwambiri’ (buku lakuti Yandikirani kwa Yehova), 7/1

Misonkhano ya “Olengeza Ufumu Achangu,” 1/15

Misonkhano ya “Patsani Mulungu Ulemerero,” 3/1

Mmene Anthu Amakhalira pa Msasa wa Anthu Othaŵa Kwawo (Dziko la Tanzania), 2/15

“Moyo Ndi Wokoma!” 1/1

Mwambo Womaliza Maphunziro a Gileadi, 6/15, 12/15

Ogwiritsa Ntchito Chinenero Chapadera (Dziko la Korea), 6/15

“Okonzeka pa Ntchito Iliyonse Yabwino,” 12/1

São Tomé ndi Príncipe, 10/15

Vidiyo Imene Imakhudza Mitima ya Achinyamata, 7/1

MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU

Achinyamata, Yendani Moyenera Yehova, 10/15

Achinyamatanu Mukupita Patsogolo Mwauzimu? 4/1

Chikondi, 7/1

Ganizani Bwino Kuti Muchite Zinthu Mwanzeru, 7/15

Khalani ndi Mtima Wopatsa, 11/1

Khalani Okhazikika, 5/15

Kuchita Zinthu Moganizira Ena, 8/1

Kufuna Yehova Mwakhama, 8/15

Kugwiritsira Ntchito Bwino Kusintha kwa Zinthu, 3/1

Kukwanitsidwa ndi Zimene Tili Nazo, 6/1

Kumvetsa Cholinga cha Kulanga, 10/1

Kuona Kuti Okhulupirira Achikulire ndi Ofunika Kwambiri, 9/1

Kupatsa Kumene Kumasangalatsa Mulungu, 6/1

“Limbikani, Ine Ndaligonjetsa Dziko Lapansi,” 3/15

“Malamulo A Wanzeru” (Miy. 13), 9/15

‘Milomo ya Ntheradi’ (Miy. 12), 3/15

‘Mulungu Akomera Mtima Wabwino’ (Miy. 12), 1/15

Mumafunikira Lamulo la M’Baibulo Nthaŵi Zonse? 12/1

“Munalandira Kwaulere, Patsani Kwaulere,” 8/1

‘Musakhale Womangidwa m’Goli ndi Wosiyana,’ 10/15

Musalekerere Mtima wa Mwana Wanu! 2/15

Mwana Wanga Azipita ku Sukulu? 3/15

Tamandani Yehova ‘Pakati pa Msonkhano,’ 9/1

Yehova Amaona Zimene Inu Mumachita? 5/1

NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA

Achinyamata Amene Amakondweretsa Mtima wa Yehova, 4/15

Achinyamatanu​—Yehova Sadzaiŵala Ntchito Yanu! 4/15

Akazi Achikristu Okhulupirika Ndi Olambira Mulungu Ofunika Kwambiri, 11/1

Akazi Amene Anakondweretsa Mtima wa Yehova, 11/1

Atumiki a Yehova Ali ndi Chiyembekezo Chenicheni (Mika), 8/15

Chitonthozo Chenicheni Chingapezeke Kuti? 5/1

Dalirani Yehova, 9/1

“Dikirani”! 1/1

Imani ndi Kupenya Chipulumutso cha Yehova! 6/1

‘Khalani Amphamvu Ndipo Limbikani Mtima!’ 3/1

Khalani Maso Kuposa Kale Lonse! 1/1

Khalani Okonzekeratu Tsiku la Yehova, 12/15

“Khalani Oyamikira,” 12/1

Khalani Wodziletsa Kuti Mudzalandire Mphoto! 10/15

‘Khalanibe M’mawu Anga,’ 2/1

Khulupirirani Yehova ndi Mtima Wanu Wonse, 3/1

Khulupirirani Yehova Panthaŵi za Mavuto, 9/1

Kodi Chikhulupiriro Chanu N’cholimba Bwanji? 1/15

Kodi Muli ndi Mtima Wodikira? 7/15

Kodi Mumakhulupiriradi Uthenga Wabwino? 1/15

Kodi Yehova Amafuna Chiyani kwa Ife? (Mika), 8/15

‘Kondanani Wina ndi Mnzake,’ 2/1

“Kondwerani mwa Yehova,” 12/1

Kristu Akulankhula ku Mipingo, 5/15

Kufatsa Ndi Khalidwe Lachikristu Lofunika Kwambiri, 4/1

Kukambirana Nkhani Zauzimu Kumalimbikitsa, 9/15

Kupirira Poyesedwa Kumalemekeza Yehova, 10/1

Kutsanzira Mulungu wa Choonadi, 8/1

Kuzunzika Chifukwa cha Chilungamo, 10/1

Lalikirani ndi Cholinga Chopanga Ophunzira, 11/15

‘Lunjikani Nawo Bwino Mawu a Mulungu,’ 11/15

Mgonero wa Ambuye Uli ndi Phindu Lanji kwa Inu? 2/15

Mmene Akristu Oyambirira Anachitira ndi Chilamulo cha Mose, 3/15

“Mubale Chipatso Chambiri,” 2/1

“Mulungu Ndiye Chikondi,” 7/1

Mumafunsa Kuti, “Ali Kuti Yehova?” 5/1

“Musaope, Kapena Kutenga Nkhaŵa,” 6/1

Muziyang’ana Ubwino wa Onse, 6/15

Mverani Zimene Mzimu Ukunena! 5/15

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuchita Chikumbutso cha Mgonero wa Ambuye? 2/15

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kupemphera Kosaleka? 9/15

Onani Ena Monga Momwe Yehova Amawaonera, 3/15

Onetsani ‘Kufatsa Konse pa Anthu Onse,’ 4/1

“Taonani, Uyu Ndiye Mulungu Wathu,” 7/1

Thandizani Ena Kulabadira Uthenga wa Ufumu, 11/15

Tidzayenda M’dzina la Yehova Mpaka Muyaya! (Mika), 8/15

Tifunika Kukhala Maso Kwambiri Tsopano, 12/15

Tiziwaona Bwanji Anthu Pamene Tsiku la Yehova Likuyandikira? 7/15

Tonthozani Amene Ali ndi Chisoni, 5/1

Tsanzirani Yehova, Mulungu Wathu Wopanda Tsankho, 6/15

Wonjezerani Kudziletsa pa Chizindikiritso Chanu, 10/15

Yehova, Mulungu wa Choonadi, 8/1

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Alexander VI (papa), 6/15

Anafunafuna Njira Yochepetsetsa (Mgwirizano wa Abale), 12/15

Baibulo Lingathandize Ukwati, 9/15

Baraki, 11/15

Chifukwa chake Mulungu Amalola Mavuto, 1/1

Chikumbutso (Mgonero wa Ambuye), 4/1

Dziko la Paradaiso, 11/15

Eusebius​—Kodi Anali “Woyamba Kulemba Mbiri ya Tchalitchi”? 7/15

Guwa la Nsembe N’lofunika Polambira? 2/15

‘Khalani ndi Chikumbumtima Chabwino,’ 5/1

Kodi Mphamvu Zoipa Zapambana? 1/15

Kodi Timafunikadi Anthu Ena? 7/15

Kufukiza, 6/1

Kukoma Mtima Kwachikondi, 4/15

Kuona Mtima, 2/1

Kusangalala Ndiponso Kukhalitsa pa Ntchito, 2/1

Kusankha Zochita, 10/15

Kuthandiza Osoŵa, 6/1

‘Kutsalima Pachothwikira’ (Mac. 26:14), 10/1

Maganizo Abwino pa Nkhani ya Ntchito, 2/1

Martin Luther, 9/15

Mkuyu, 5/15

Moyo Wauzimu, 4/15

‘Mpingo Woona’ Umodzi Wokha? 9/1

Mukufuna Kuti Anthu Adzakukumbukireni Ngati Munthu Wotani? 8/15

N’chiyani Chinaichitikira? (Nofi ndi No), 7/1

Ndani Tingamukhulupirire? 11/1

Nkhani ya Nowa, 5/15

‘Solomo Sanavala Monga Limodzi la Ameneŵa,’ 6/1

Tatian Anali Woikira Kumbuyo Chikristu Kapena Anali Wopanduka? 5/15

Thandizo kwa Anthu Osauka, 9/1

Ugariti​—Mzinda Wakale, 7/15

Ukwati wa Boazi ndi Rute, 4/15

Umphaŵi, 3/15, 8/1

Yakobo, 10/15

Zimene Mbalame Zingatiphunzitse, 6/15

Zitsime, 12/1

YEHOVA

Amaganizira Anthu Wamba, 4/15

Amaganiziradi Anthu? 10/1

Amaona Zimene Inu Mumachita? 5/1

Chifukwa Chiyani Tiyenera Kukhulupirira Mulungu? 12/1

Mafunso Ofunika Kufunsa Mulungu, 5/1

Wofunika Kum’dziŵa, 2/15

YESU KRISTU

Anakhalako Padziko Lapansi? 6/15

Makolo ndi Achibale, 12/15

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena