Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 12/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2010
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2010
w10 12/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

December 15, 2010

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

January 31, 2011–February 6, 2011

Khalani Odzipereka pa Kulambira Koona

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 10, 17

February 7-13, 2011

‘Inoyo Ndiyo Nthawi Yeniyeni Yovomerezeka’

TSAMBA 11

NYIMBO ZOIMBA: 44, 47

February 14-20, 2011

Pezani Madalitso Kudzera mwa Mfumu Yotsogoleredwa ndi Mzimu wa Mulungu

TSAMBA 16

NYIMBO ZOIMBA: 30, 5

February 21-27, 2011

Imbirani Yehova

TSAMBA 20

NYIMBO ZOIMBA: 28, 43

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 MASAMBA 7-15

M’nkhani zimenezi tiona mmene Yesu anasonyezera kudzipereka ndiponso zimene tikuphunzira pa chitsanzo chake. Tionanso kuti n’chifukwa chiyani tiyenera kukhala odzipereka kwambiri mu utumiki makamaka masiku ano. Ndiponso tiphunzira kuti n’chifukwa chiyani tinganene kuti inoyo ndiyo nthawi yovomerezeka.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 MASAMBA 16-20

Tikukhala m’nthawi imene ulamuliro wa anthu ukulephera. Nkhani iyi itithandiza kuona chifukwa chake Yehova wasankha Yesu Khristu kukhala wolamulira anthu ndiponso madalitso ambirimbiri amene tingapeze ngati tigonjera Khristu.

NKHANI YOPHUNZIRA 4 MASAMBA 20-24

N’chifukwa chiyani tinganene kuti kuimba n’kofunika kwambiri pa kulambira kwathu ndiponso n’kogwirizana ndi Malemba? Nkhani iyi itithandiza kupeza yankho la funso limeneli. Itithandizanso kuona zimene aliyense payekha angachite kuti aziimba.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

Kodi Mwana Wanu Angayankhe Bwanji? 3

Kodi Mukukumbukira? 6

Ukalamba Sungatilephe retse Kutumikira Mulungu 25

Ndaona Mphamvu ya Choonadi cha M’Baibulo 26

Mafunso Ochokera kwa Owerenga 30

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2010 32

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena