Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 8/1 tsamba 24-25
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Nkhani Yofanana
  • Phunziro 3
    Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kolalikira
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda—2012
w12 8/1 tsamba 24-25

Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo

ANA AZAKA ZOSAPITIRIRA ZITATU

Kalebe wamva zoti mnzake akudwala.

Iye akuti: “Ndadziwa chochita.

Ndimulembera kalata kuti ndimulimbikitse, ndipo kenako ndikam’patsa.”

Muzisonyeza ena chifundo ndipo nonse mudzakhala osangalala. 1 Petulo 3:8

ZOTI MAKOLO ACHITE

Muuzeni mwana wanuyo kuti aloze:

Nyumba

Tebulo

Kalebe

Dzuwa

Mbalame

Mtengo

Tchulani munthu amene akudwala ndipo kambiranani ndi mwanayo mmene mungamulimbikitsire.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena