Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w16 August tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
w16 August tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

3 Mbiri ya Moyo Wanga—Ndimasangalala Chifukwa Chothandiza Ena

MLUNGU WA SEPTEMBER 26, 2016–OCTOBER 2, 2016

8 Kodi Ukwati Unayamba Bwanji Nanga Cholinga Chake N’chiyani?

MLUNGU WA OCTOBER 3-9, 2016

13 Kodi Mungatani Kuti Banja Lanu Liziyenda Bwino?

Nkhani yoyamba ikufotokoza mmene ukwati unayambira ndiponso zimene Chilamulo cha Mose chinkanena pa nkhaniyi. Ikufotokozanso malangizo okhudza ukwati amene Yesu anapereka kwa Akhristu. Nkhani yachiwiri ikufotokoza udindo wa mwamuna komanso wa mkazi m’banja.

18 Muzifufuza Chuma Chamtengo Wapatali Kuposa Golide

MLUNGU WA OCTOBER 10-16, 2016

20 Kodi Tingatani Kuti Tizichita Zambiri M’gulu la Yehova?

MLUNGU WA OCTOBER 17-23, 2016

25 Kodi Kuphunzitsa Ena N’kofunika Bwanji?

Tonsefe tikusangalala kuona kuti ntchito yolalikira ikuyenda bwino. Koma kodi tikudziwa kuti zimenezi zikupangitsa kuti m’gulu la Yehova mukhale ntchito yambiri? Kodi tingatani kuti tizichita zambiri m’gulu la Yehova? Nanga tingathandize bwanji amene timaphunzira nawo kuti nawonso azichita zambiri? N’chifukwa chiyani tiyenera kuphunzitsa ena? M’nkhanizi tikambirana mayankho a mafunso amenewa.

30 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

31 Kale Lathu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena