Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/09 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 23

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 23
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 23
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 2/09 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa February 23

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 23

Nyimbo Na. 22

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 15 ndime 1-7

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 32-35

Kubwereza za m’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 1

Mph. 5: Zilengezo. Tchulani mabuku ogawira m’mwezi wa March.

Mph. 10: Konzekerani Kugawira Nsanja ya Olonda ya March 1 ndi Galamukani! ya March. Pambuyo pofotokoza mwachidule zimene zili m’magaziniwo, pemphani omvera kuti atchule nkhani zimene zingasangalatse anthu a m’gawo lanu ndiponso chifukwa chake. Pogwiritsa ntchito nkhani za m’magaziniwo, pemphani omvera kuti atchule funso limene angafunse kuti ayambitse makambirano komanso lemba limene angawerenge asanagawire magaziniwo. Malizani ndi chitsanzo chosonyeza mmene tingagawirire magazini iliyonse.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Kodi Mukugwiritsa Ntchito Kabuku ka Kusanthula Malemba Tsiku ndi Tsiku? Nkhani ndi kukambirana ndi omvera kuchokera pa mawu oyamba a m’kabuku ka Kusanthula Malemba Tsiku ndi Tsiku—2009. Kambiranani ubwino wokhala ndi nthawi yowerenga Lemba la tsiku ndi ndemanga yake tsiku lililonse. Pemphani omvera kuti afotokoze za nthawi imene amachita lemba latsiku, mmene amachitira ndiponso phindu limene apeza.

Nyimbo Na. 38

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena