Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/09 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 25

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 25
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 25
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 5/09 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa May 25

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 25

Nyimbo Na. 74

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 19 ndime 18-23 ndi bokosi la patsamba 198

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Eksodo 34–37

Na. 1: Eksodo 37:1-24

Na. 2: Kodi Ndi Bwino Kuchita Ndewu? (lr-CN mutu 19)

Na. 3: Kodi Khalidwe Lolekerera Ndi Lotani, Ndipo N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kulipewa?

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 193

Mph.5: Zilengezo.

Mph.10: Konzekerani Kugawira Magazini ya Nsanja ya Olonda ya June 1 ndi Galamukani! ya June. Fotokozani mwachidule mfundo za m’magaziniwa ndipo funsani omvera kuti atchule nkhani zimene akonzekera kudzagwiritsa ntchito pogawira magaziniwa ndipo anene chifukwa chake. Kodi ndi mafunso komanso malemba ati amene angagwiritse ntchito pogawira magaziniwa? Chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungagawire magazini iliyonse m’gawo lanu.

Mph.10: Kuchitira Umboni za Yesu. Nkhaniyi ili m’buku la Sukulu ya Utumiki kuyambira pakamutu komwe kali patsamba 275 ndime 1-3 ndiponso tsamba 276 ndime 1.

Mph.10: “Gwiritsani Ntchito Bwino Mabuku Athu.” Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Dziwitsani mpingo za kusiyana kwa chiwerengero cha mabuku amene mumalandira ndi chiwerengero chimene anthu amachitira lipoti kuti agawira mu utumiki.

Nyimbo Na. 123

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena