Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/09 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 1

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 1
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 1
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 5/09 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa June 1

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 1

Nyimbo Na. 26

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 20 ndime 1-12

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Eksodo 38-40

Na. 1: Eksodo 40:1-19

Na. 2: Kodi Nthawi Zonse Mumafuna Kukhala Woyamba? (lr-CN mutu 20)

Na. 3: Kodi Anthu Onse Adzachiritsidwa? (rs-CN tsa. 169 ndime 5 mpaka tsa. 170 ndime 2)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 129

Mph.5: Zilengezo.

Mph.10: Thandizani Ena Kupita Patsogolo. Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, pakamutu koyambira pa tsamba 187. Mwachidule funsani mpainiya kapena wofalitsa amene wathandiza atsopano kupita patsogolo.

Mph.10: Zosowa za pampingo.

Mph.10: Kodi Tinachita Zotani? Nkhani yokambirana ndi omvera. Yamikirani mpingo chifukwa cha kuwonjezera utumiki panyengo ya Chikumbutso, ndipo tchulani zimene mpingo unachita. Pemphani omvera kufotokoza zimene anakumana nazo pogawira timapepala toitanira anthu ku Chikumbutso kapena potumikira monga mpainiya wothandiza.

Nyimbo Na. 53

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena