Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/09 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 21

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 21
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 21
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 9/09 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa September 21

MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 21

Nyimbo Na. 69

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 26 ndime 8-15

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Numeri 30-32

Na. 1: Numeri 32:1-15

Na. 2: Kodi Chimachitika ndi Chiyani Tikamwalira? (lr-CN mutu 34)

Na. 3: Kodi Akhristu Onse Ali ndi Chiyembekezo Chopita Kumwamba? (rs-CN tsa. 206 ndime 1-3)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 141

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Konzekerani Kugawira Nsanja ya Olonda ya October 1 ndi Galamukani! Yapadera ya October. Fotokozani mwachidule zimene zili m’magaziniwa. Pemphani omvera kuti atchule nkhani za m’magazini yapadera ya Galamukani! zimene anthu ambiri a m’gawo lanu angazikonde. Funsani mafunso mpainiya amene ali ndi luso logawira magazini ndipo achite chitsanzo cha mmene angagawirire Galamukani! yapadera.

Mph. 10: Ngati Wina Atanena Kuti, ‘Sindili Wokondwerera.’ Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Kukambitsirana tsamba 16. Pemphani wofalitsa kuti achite chitsanzo pogwiritsa mfundo imodzi kapena ziwiri za patsambali.

Mph. 10: “Kugwiritsa Ntchito Baibulo Mwaluso.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 107

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena