Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/10 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 26

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 26
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 26
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 4/10 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa April 26

MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 26

Nyimbo Na. 21

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 6 ndime 1-9

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Samueli 26-31

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 24

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Konzekerani Kugawira Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! Choyamba chitani chitsanzo. Mpainiya asonyeze zimene angachite pogawira magazini atsopano a Nsanja ya Olonda kapena Galamukani! Kenako pemphani omvera kuti atchule mwachidule nkhani, mafunso ndiponso malemba amene angagwiritse ntchito pogawira magaziniwo.

Mph. 20: Gwirani Nawo Ntchito Yaikulu Yofunafuna Anthu. Nkhani yochokera m’buku la Gulu, kuyambira patsamba 95 pakamutu kakuti, “Kufunafuna Oyenerera.” Pemphani omvera kuyankha mafunso otsatirawa. N’chifukwa chiyani tiyenera kukhala ndi maganizo abwino polankhula ndi anthu a m’gawo lathu? Kodi kukhala ndi maganizo abwino kungathandize bwanji utumiki wathu kuyenda bwino? Funsani mwachidule wofalitsa mmodzi amene khama lake lathandiza kuti akhale ndi zotsatira zabwino mu utumiki.

Nyimbo Na. 9

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena