Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/10 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 3

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 3
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 3
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 4/10 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa May 3

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 3

Nyimbo Na. 4

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 6 ndime10-15 ndi bokosi la patsamba 67

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Samueli 1-3

Na. 1: 2 Samueli 2:12-23

Na. 2: Kodi Yesu Ankagwiritsa Ntchito Dzina la Mulungu pa Utumiki Wake?

Na. 3: Kodi Maholide Okumbukira “Mizimu ya Akufa” Anakhazikitsidwa Chifukwa Chiyani? (rs tsa. 244 ndime 1–tsa. 245 ndime 1)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 31

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Ngati Mwininyumba wanena kuti, ‘Simumakhulupirira Yesu.’ Nkhani yokambirana ndi omvera kuchokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 433.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Sangalalani Pochita Nawo Ulaliki wa Kagulu. Kambiranani ndi omvera kuchokera m’buku la Gulu, patsamba 108 ndime 1-3. Pemphani woyang’anira utumiki kuti anene masiku ndiponso malo okumanira pokonzekera utumiki wakumunda. Pemphani omvera kutchula madalitso amene apeza chifukwa chochita nawo ulaliki umenewu ndiponso chifukwa cholalikira ndi ofalitsa a m’gulu lawo la utumiki wa kumunda.

Nyimbo Na. 17

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena