Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/10 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 27

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 27
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 27
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 9/10 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa September 27

MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 27

Nyimbo Na. 47

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo

lv mutu 12 ndime 15-22, ndi bokosi patsamba 140

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu

Kuwerenga Baibulo: 2 Mafumu 23-25

Na. 1: 2 Mafumu 23:1-7

Na. 2: Kodi Ndi Zikhulupiriro za Mboni za Yehova Ziti Zimene Zimawapangitsa Kukhala Osiyana ndi Zipembedzo Zina? (rs-CN tsa. 270 ndime 3–tsa. 272 ndime 3)

Na. 3: Kodi Akhristu Oona Angaonetse Kuwala Kwawo M’njira Ziti? (Mat. 5:14-16)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 45

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 15: Konzekerani Kugawira Magazini a October. Nkhani yokambirana. Fotokozani nkhani zimene zili m’magaziniwo kwa mphindi imodzi kapena ziwiri. Ndiyeno sankhani nkhani ziwiri kapena zitatu ndi kupempha omvera kuti atchule mafunso ndi malemba okhudza nkhanizo amene angagwiritse ntchito pogawira magaziniwo. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungagawirire magaziniwo.

Mph. 15: “Kodi Muyambitsa Nawo Phunziro la Baibulo M’mwezi wa October?” Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri.

Nyimbo Na. 10

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena