Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/10 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 4

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 4
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 4
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 9/10 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa October 4

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 4

Nyimbo Na. 10

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 13 ndime 1-4, ndi mabokosi pamasamba 148-149, 158-159

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mbiri 1-4

Na. 1: 1 Mbiri 1:1-27

Na. 2: Zimene Kukhala Wodzetsa Mtendere Kumatanthauza (1 Pet. 3:10-12)

Na. 3: Kodi Mboni za Yehova Ndi Chipembedzo cha ku America, Nanga Amapeza Bwanji Ndalama Zoyendetsera Ntchito Yawo? (rs-CN tsa. 272 ndime 4–tsa. 273 ndime 3)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 11

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Chifukwa Chimene Timaperekera Lipoti la Utumiki Wathu Wakumunda. Nkhani yokambidwa ndi mlembi yochokera m’buku la Gulu, tsamba 88, ndime 1, mpaka tsamba 90, ndime 1.

Mph. 8: Zosowa za pampingo.

Mph. 12: Kodi Mungakonzekere Bwanji Kuthana ndi Mavuto a Kusukulu? Kukambirana ndi omvera. Pemphani omvera kuti afotokoze ena mwa mavuto amene Akhristu achinyamata amakumana nawo kusukulu. Fotokozani mmene makolo angagwiritsirire ntchito index, mabuku a Achinyamata Akufunsa ndiponso zofalitsa zina pa Kulambira kwa Pabanja kukonzekeretsa ana awo kuti athane ndi mayesero ndiponso kuti azifotokoza zimene amakhulupirira. (1 Pet. 3:15) Sankhani nkhani imodzi kapena ziwiri, ndipo fotokozani mfundo zothandiza zimene zikupezeka m’zofalitsa zathu. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene anachita kuti athe kulalikira kusukulu.

Nyimbo Na. 2

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena