Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/11 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 29

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 29
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 29
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 8/11 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa August 29

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 29

Nyimbo Na. 45 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu  12, ndime 1-7 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Masalimo 110–118 (Mph. 10)

Kubwereza za M’sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 32

Mph. 10: Zilengezo. Pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chimene chili patsamba 8, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingayambitsire phunziro la Baibulo, Loweruka loyamba m’mwezi wa September. Limbikitsani onse kuti ayesetse kuyambitsa maphunziro. Kambani nkhani pogwiritsa ntchito mutu wakuti “Gawirani Magazini Kapena Kabuku Kakale Kogwirizana Ndi Zimene Munthu Alinazo Chidwi.”

Mph. 15 Akhama mu Utumiki Ngakhale Kuti ndi Okalamba. Nkhani yokambirana, yochokera mu Nsanja ya Olonda ya June 1, 2007, tsamba 28 ndi 29, ndime 10 mpaka 15. Pemphani omvera kufotokoza zimene aphunzira mu nkhaniyi.

Mph. 10 Konzekerani Kugawira Magazini M’mwezi wa September. Nkhani yokambirana. Fotokozani zimene zili m’magaziniwo kwa mphindi imodzi kapena ziwiri. Kenako sankhani mitu iwiri kapena itatu, ndipo funsani omvera kuti afotokoze mafunso ndiponso malemba amene angagwiritse ntchito pogawira magaziniwo. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungagawire magazini iliyonse.

Nyimbo Na. 31 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena