Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/11 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 3

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 3
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 3
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 9/11 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa October 3

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 3

Nyimbo Na. 6 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 13 ndime 18-21 ndi bokosi patsamba 138 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Miyambo 1-6 (Mph. 10)

Na. 1: Miyambo 6:1-19 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Lemba la Aroma 8:26, 27 Limatitsimikizira Motani Kuti Mulungu Amatikonda? (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Ufumu wa Mulungu Udzayembekezera Kaye Kuti Anthu Onse Padziko Lapansi Atembenuke Usanabwere?—rs tsa. 381 ndime 5 mpaka tsa. 382 ndime 1 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 29

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kodi Taphunzira Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Luka 5:12, 13 ndi Luka 8:43-48. Kambiranani mmene nkhani zopezeka pa malembawa zingatithandizire mu utumiki.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Sonyezani Khalidwe Labwino mu Utumiki. (2 Akor. 6:3) Nkhani yokambirana. Gwiritsani ntchito mafunso otsatirawa pokambirana. (1) N’chifukwa chiyani tiyenera kusonyeza makhalidwe abwino tikamalalikira? (2) Kodi tingasonyeze bwanji makhalidwe abwino (a) gulu lathu likafika m’gawo limene timalalikira? (b) tikamayenda nyumba ndi nyumba? (c) tikafika pakhomo la mwininyumba? (d) mnzathu akamalalikira? (e) mwininyumba akamalankhula? (f) tikapeza mwininyumba ali wotanganidwa kapena ngati nyengo siili bwino? (g) ngati mwininyumba ndi wamwano?

Nyimbo Na. 16 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena