Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/11 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 21

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 21
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 21
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 11/11 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa November 21

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 21

Nyimbo Na. 50 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 16 ndime 1-6 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Mlaliki 7-12 (Mph. 10)

Na. 1: Mlaliki 9:13–18; 10:1-11 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Chikondi Sichichita Nsanje—1 Akor. 13:4 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Chizindikiro Cha Masiku Otsiriza Chimawakhudza Bwanji Akhristu Oona?—rs tsa. 265 ndime 2 ndi 3 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 52

Mph. 5: Zilengezo. Bokosi la Mafunso. Nkhani.

Mph. 15: Anazunzidwa Chifukwa Chochitira Umboni. (Luka 21:12, 13) Nkhani yokambirana yochokera mu Nsanja ya Olonda ya March 1, 2009, tsamba 12-13, ndime 1 mpaka 10. Komanso kambiranani ndime 2 ndi 3 zokha patsamba 14. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene aphunzirapo.

Mph. 10: Magazini Ogawira m’Mwezi wa December. Nkhani yokambirana. Kambiranani nkhani zina za m’magaziniwa ndipo chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri.

Nyimbo Na. 33 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena