Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/12 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 20

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 20
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 20
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 8/12 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa August 20

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 20

Nyimbo Na. 44 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 11 ndime 1-4 ndi mabokosi a patsamba 84, 86 ndi 87 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Ezekieli 32-34 (Mph. 10)

Na. 1: Ezekieli 34:15-28 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Ndi Malemba Ati Amene Amachititsa Kuti Akhristu Asamachite Nawo Miyambo Yosonyeza Kukonda Dziko Lako?—rs tsa. 372 ndime 3 mpaka tsa. 374 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Tinganene Kuti Mapemphero Ochokera Mumtima Amafuna Zambiri?—Sal. 145:18; Mat. 22:37 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 76

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Ngati Wina Wanena Kuti: Ndimakhulupirira Kuti Zamoyo Zinachita Kusintha Kuchokera ku Zinthu Zina. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Kukambitsirana patsamba 104, ndime 3 mpaka kumapeto kwa tsamba 106. Chitani chitsanzo chachidule chosonyeza mmene tingayankhire ngati wina atanena kuti, ‘Ndimakhulupirira kuti Mulungu analenga munthu pochita kusandutsa chinthu china chamoyo n’kukhala munthu.’

Mph. 10: Muzilimbikitsana. (Aroma 1:12) Nkhani yokambirana yochokera mu Nsanja ya Olonda ya February 15, 2012, tsamba 20 ndime 8 ndi tsamba 21, ndime 8 ndi 9. Yamikirani mpingo chifukwa cha khama limene umachita mu utumiki.

Mph. 10: “Tetezani Maganizo Anu.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 70 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena