Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/14 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 14

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 14
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 14
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 7/14 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa July 14

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 14

Nyimbo Na. 47 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 13 ndime 20-26 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Levitiko 21-24 (Mph. 10)

Na. 1: Levitiko 23:1-14 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Zoti Anthu Onse Adzapulumuka Si za M’Malemba—rs tsa. 94 ndime 3 (Mph. 5)

Na. 3: Muzigwiritsa Ntchito Mwanzeru Nthawi Yovomerezeka Imene Muli Nayo Potumikira Mulungu—2 Akor. 6:2; Aheb. 3:7-8 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 45

Mph. 10: Konzekerani Kudzagwira Nawo Ntchito Yapadera mu August. Gawani kapepala katsopano kakuti, Mayankho a Mafunso Ofunika Kwambiri Okhudza Moyo kwa onse amene alibe kapepalaka. Pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chomwe chili patsamba 8, chitani zitsanzo ziwiri zosonyeza mmene tingagawirire kapepalaka. Chitsanzo choyamba chisonyeze mmene tingagawirire kapepalaka kwa anthu onse. Chachiwiri chisonyeze zimene tinganene ngati munthu amene tamugawira kapepalaka wasonyeza kuti akufuna kudziwa zambiri. Limbikitsani onse kuti adzagwire nawo ntchito yapadera imeneyi.

Mph. 5: Muzigwiritsa Ntchito Kabuku Kakuti, Kuphunzira Malemba Tsiku ndi Tsiku. Nkhani yokambirana. Pemphani omvera kuti anene nthawi imene amapanga lemba la tsiku komanso mmene apindulira.

Mph. 15: “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki​—Mmene Tingayambire Ulaliki Wamwamwayi.” Nkhani yokambirana. Chitani chitsanzo chimodzi.

Nyimbo Na. 107 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena