Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/15 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 23

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 23
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 23
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 2/15 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa February 23

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 23

Nyimbo Na. 109 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 9 ndime 1-7 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Oweruza 19-21 (Mph. 8)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: Khalani “Odzipereka pa Ntchito Zabwino”​—Tito 2:14.

Nyimbo Na. 75

Mph. 10: Zofunika pampingo.

Mph. 10: Khalani Odzipereka pa Kulambira Koona Ngati Yesu. Nkhani yochokera mu Nsanja ya Olonda ya May 15, 2013 tsamba 8 ndime 2 komanso ya December 15, 2010 tsamba 9-11 ndime 12-16. Fotokozani chifukwa chake ntchito yolalikira ndi imodzi mwa “ntchito zabwino” moti Mkhristu aliyense ayenera kuona kuti ndi mwayi kugwira nawo ntchitoyi. (Tito 2:14) Fotokozani mmene kudziwa choonadi kumatithandizira kuti tizifunitsitsa kuuza ena uthenga wabwino modzipereka komanso kuphunzira nawo Baibulo. Yamikirani mpingo wonse chifukwa cha kudzipereka kwawo pa ntchito zabwino.

Mph. 10: “Tizigwira Modzipereka Ntchito Yothandiza Ena Kudziwa Zoona Zokhudza Yesu.” Nkhani yokambirana. Chitani chitsanzo chosonyeza wofalitsa akuchita zomwe zili mu “Chitsanzo 1,” mu Nsanja ya Olonda ya May 15, 2014, tsamba 8 ndime 8. Anenenso chitsanzo chomwe chili patsamba 9 ndime 13.

Nyimbo Na. 5 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena