Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsamba 2
  • Chizindikiro Chosonyeza Kuti Aisiraeli Adzabwerera Kwawo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chizindikiro Chosonyeza Kuti Aisiraeli Adzabwerera Kwawo
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Mbali Yodabwitsa ya Ubwino wa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1989
  • Yehova Ndiye Chitsanzo Chachikulu Pankhani Yosonyeza Ubwino
    Nsanja ya Olonda—2002
  • “Ubwino Wake Ndi Waukulu Kwambiri!”
    Yandikirani Yehova
  • Ubwino Waukulu wa Yehova
    Nsanja ya Olonda—1991
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 May tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YEREMIYA 32-34

Chizindikiro Chosonyeza Kuti Aisiraeli Adzabwerera Kwawo

Losindikizidwa

32:9-14

  • Yeremiya anatsatira malamulo ofunika pogula munda.

    Pamene Yeremiya ankafuna kugula munda, anayeza ndalama kenako anapereka chikalata chochitira umboni ndipo anasunga chikalatacho mumbiya

33:10, 11

  • Yehova anasonyeza kuti ndi wabwino polonjeza anthu ake omwe anali ku ukapolo kuti akamvera malangizo ake, adzawakhululukira ndipo adzabwerera ku Isiraeli.

    Mapu osonyeza pamene pali Yerusalemu komanso ku Anatoti, dera limene Yeremiya ankakhala

Kodi Yehova wasonyeza bwanji kuti ndi wabwino kwa inuyo?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena