Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb25 May tsamba 14
  • June 23-29

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • June 23-29
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
mwb25 May tsamba 14

JUNE 23-29

MIYAMBO 19

Nyimbo Na. 154 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Muzikhala Bwenzi Lenileni kwa Abale ndi Alongo Anu

(10 min.)

Muzinyalanyaza zolakwa zawo (Miy 19:11; w23.11 12-13 ¶16-17)

Muziwathandiza pamene akufunika thandizo (Miy 19:17; w23.07 9-10 ¶10-11)

Muziwasonyeza chikondi chokhulupirika (Miy 19:22; w21.11 9 ¶6-7)

Chithunzi chosonyeza abale ndi alongo akumwetulira.

CHITSANZO: Zimene mumachita ndi abale ndi alongo anu zili ngati zithunzi. Muzisunga zithunzi zabwino zokha zomwe tingaziyerekezere ndi makhalidwe awo abwino.

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Miy 19:21—Kodi nthawi zonse tiziganizira chiyani tikamapereka malangizo? (it-1 515)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Miy 19:1-20 (th phunziro 2)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Popanda kutchula mfundo ya m’Baibulo, pezani njira yomwe ingathandize munthu amene mukukambirana naye kudziwa kuti ndinu wa Mboni za Yehova. (lmd phunziro 2 mfundo 4)

5. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Pa ulendo wapita, munthuyo anakuuzani kuti amasangalala ndi chilengedwe. (lmd phunziro 9 mfundo 4)

6. Nkhani

(5 min.) lmd zakumapeto A mfundo 10—Mutu: Mulungu Ali ndi Dzina. (th phunziro 20)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 40

7. Zofunika Pampingo

(15 min.)

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 28 ¶1-7

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 61 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena