Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • wp25 No. 1 tsamba 2
  • Mawu Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2025
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Nkhondo Komanso Zachiwawa Zimatikhudza Bwanji Tonsefe?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2025
  • Mtendere Weniweni—Kodi Udzachokera Kuti?
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Kodi Nkhondo Zidzakhalako Mpaka Liti?
    Galamukani!—1999
  • N’chifukwa Chiyani Nkhondo Komanso Zachiwawa Zikuchitikabe Padzikoli?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2025
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2025
wp25 No. 1 tsamba 2

Mawu Oyamba

Kodi mumafunitsitsa mutakhala m’dziko lopanda nkhondo komanso zachiwawa? Anthu ambiri amakhulupirira kuti zimenezi n’zosatheka. Baibulo limanena chifukwa chake ndi zosatheka kuti anthu athetse nkhondo. Limafotokozanso chifukwa chake muyenera kukhulupirira kuti posachedwapa padziko lonse padzakhala mtendere.

M’magaziniyi, mawu akuti “nkhondo” ndi “zachiwawa” akuimira mikangano ya pakati pa mayiko komanso magulu andale amene amagwiritsira ntchito zida zankhondo pomenyana. Mayina a anthu ena amene atchulidwa m’magaziniyi asinthidwa.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena