Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ijwbq nkhani 17
  • Kodi Baibulo Limaloleza Kuthetsa Ukwati?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Baibulo Limaloleza Kuthetsa Ukwati?
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Yankho la m’Baibulo
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Chisudzulo—Kodi Nchiyani Chimene Baibulo Limanena Kwenikweni?
    Nsanja ya Olonda—1988
  • Kusudzulana
    Galamukani!—1999
  • Tizilemekeza “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Onani Zambiri
Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
ijwbq nkhani 17
Mwamuna ndi mkazi wake akuganiza zothetsa ukwati wawo

Kodi Baibulo Limaloleza Kuthetsa Ukwati?

Yankho la m’Baibulo

Baibulo limaloleza kuthetsa ukwati. Komabe, Yesu anatchula chifukwa chimodzi chokha chovomerezeka chimene chingachititse kuti banja lithe. Iye anati: “Aliyense wosiya mkazi wake n’kukwatira wina wachita chigololo, kupatulapo ngati wamusiya chifukwa cha dama [kugonana ndi munthu amene si mkazi kapena mwamuna wake].”—Mateyu 19:9.

Mulungu amadana ndi anthu amene amathetsa banja lawo mwachinyengo. Iye adzalanga munthu aliyense amene amasiya mwachinyengo mkazi kapena mwamuna wake n’cholinga choti apezenso munthu wina woti akwatirane naye.—Malaki 2:13-16; Maliko 10:9.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena