Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 2
  • Tikuyamikani Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikuyamikani Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tikukuthokozani Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tikuyamikani, Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kodi Umakumbukira Kunena Kuti Zikomo?
    Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 2

Nyimbo 2

Tikuyamikani Yehova

Losindikizidwa

(1 Atesalonika 5:18)

1. Tikuyamikani Yehova M’lungu,

Mumatipatsa kuwala kwanu.

Tikuyamika mwayi wa pemphero,

Kuti tinene mavuto athu.

2. Tikuyamika potumiza Yesu

Amene anagonjetsa dziko.

Tikuyamikani potithandiza

Kukwaniritsa lonjezo lathu.

3. Tikuyamika chifukwa cha mwayi

Wolalikira za dzina lanu.

Tiyamika mudzathetsa mavuto,

Madalitso anu sadzathadi.

(Onaninso Sal. 50:14; 95:2; 147:7; Akol. 3:15.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena