Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 152
  • Malo Amene Adzachititsa Kuti Mulemekezedwe

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Malo Amene Adzachititsa Kuti Mulemekezedwe
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 152

NYIMBO 152

Malo Amene Adzachititsa Kuti Mulemekezedwe

Losindikizidwa

(1 Mafumu 8:27; 1 Mbiri 29:14)

  1. 1. Yehova, wolenga kumwamba,

    M’mwamba simungakwanemo,

    Ngakhalenso pano padziko.

    Koma mwatipatsa mzimu.

    Anthu anu akongoletsa

    Malo olambirirawa.

    Timadzipereka n’kumatumikira

    Mosangalala.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Zonsetu Yehova

    Munatipatsa ndinu.

    Zomwe tikupereka

    Mwatipatsa ndinu.

    (KOLASI)

    Tikuthokozatu zonsezi,

    Poimba mokweza mawu.

    Ndi malo omwe mwatipatsa

    Tidikira madalitso.

  2. 2. Yehova munadziwa ndithu

    Tinkafunika malowa,

    Adzathandiza anthu anu

    Kuyendabe m’njira zanu.

    Pali ntchito yoti tigwire.

    Malowa adzathandiza,

    Pogwiratu ntchito ya Yesu

    N’kuyendabe ndi gululi.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Tim’patse zabwino

    Nthawi ndi chuma chathu.

    Ndinu woyenera kulandira

    Zonsezi.

    (KOLASI)

    Tikuthokozatu zonsezi,

    Poimba mokweza mawu.

    Ndi malo omwe mwatipatsa

    Tidikira madalitso.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena