Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm23 tsamba 4-5
  • Loweruka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Loweruka
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2023
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Masana
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2023
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2017
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2023
CO-pgm23 tsamba 4-5
Zithunzi: Zina zomwe zili mupulogalamu ya Loweruka. 1. Banja likucheza ndi ena mosangalala pa vidiyokomfelensi. 2. Mfumu ikuganizira. 3. Bambo ali ndi mwana wake kumsika.

Loweruka

“Khalani oleza mtima kwa onse” 1 Atesalonika 5:14

M’Mawa

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 58 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YOSIYIRANA: ‘Timasonyeza Kuti Ndife Atumiki a Mulungu . . . mwa Kukhala Oleza Mtima’

    • • Tikamalalikira (Machitidwe 26:29; 2 Akorinto 6:4, 6)

    • • Tikamaphunzira Baibulo ndi Anthu (Yohane 16:12)

    • • Tikamalimbikitsana (1 Atesalonika 5:11)

    • • Tikamatumikira Monga Mkulu (2 Timoteyo 4:2)

  • 10:30 Muzileza Mtima Chifukwa Inunso Munasonyezedwa Kuleza Mtima (Mateyu 7:1, 2; 18:23-35)

  • 10:50 Nyimbo Na. 138 ndi Zilengezo

  • 11:00 NKHANI YOSIYIRANA: ‘Moleza Mtima, Muzilolerana M’chikondi’

    • • Achibale Omwe Si a Mboni (Akolose 4:6)

    • • Mwamuna Kapena Mkazi Wanu (Miyambo 19:11)

    • • Ana Anu (2 Timoteyo 3:14)

    • • Achibale Amene Akudwala Kapena Omwe Ndi Achikulire (Aheberi 13:16)

  • 11:45 NKHANI YA UBATIZO: Kuleza Mtima kwa Yehova Kumatithandiza Kuti Tidzapulumuke (2 Petulo 3:13-15)

  • 12:15 Nyimbo Na. 75 ndi Kupuma

Masana

  • 1:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:45 Nyimbo Na. 106

  • 1:50 N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kupewa Kusangalala ndi Zinthu Zosakhalitsa? (1 Atesalonika 4:3-5; 1 Yohane 2:17)

  • 2:15 NKHANI YOSIYIRANA: “Munthu Woleza Mtima Ndi Wabwino Kuposa Munthu Wodzikuza”

    • • Muzitsanzira Abele, Osati Adamu (Mlaliki 7:8)

    • • Muzitsanzira Yakobo, Osati Esau (Aheberi 12:16)

    • • Muzitsanzira Mose, Osati Kora (Numeri 16:9, 10)

    • • Muzitsanzira Samueli, Osati Sauli (1 Samueli 15:22)

    • • Muzitsanzira Yonatani, Osati Abisalomu (1 Samueli 23:16-18)

  • 3:15 Nyimbo Na. 87 ndi Zilengezo

  • 3:25 VIDIYO: ‘Muzilola Kuti Yehova Akutsogolereni’​—Mbali Yoyamba (Salimo 37:5)

  • 3:55 “Pozunzidwa, Timapirira” Moleza Mtima (1 Akorinto 4:12; Aroma 12:14, 21)

  • 4:30 Nyimbo Na. 79 ndi Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena