Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm24 tsamba 6-7
  • Lamlungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lamlungu
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Nkhani Yofanana
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2020
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2017
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
CO-pgm24 tsamba 6-7
Zithunzi: Zimene zili mupulogalamu ya Lamlungu. 1. Zekariya ndi Elizabeti. 2. Yosefe wanyamula Yesu mu shopu imene amagwiriramo ntchito ya ukalipentala. 3. Yesu akuyang’ana padziko lapansi ali kumwamba.

Lamlungu

“. . . kenako mapeto adzafika”​—Mateyu 24:14

M’mawa

  • 8:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 8:30 Nyimbo Na. 84 Komanso Pemphero

  • 8:40 NKHANI YOSIYIRANA: Muzitsanzira Anthu Amene Ankakhulupirira Uthenga Wabwino

    • • Zekariya (Aheberi 12:5, 6)

    • • Elizabeti (1 Atesalonika 5:11)

    • • Mariya (Salimo 77:12)

    • • Yosefe (Miyambo 1:5)

    • • Simiyoni ndi Ana (1 Mbiri 16:34)

    • • Yesu (Yohane 8:31, 32)

  • 10:05 Nyimbo Na. 65 Komanso Zilengezo

  • 10:15 NKHANI YA ONSE: N’chifukwa Chiyani Sitimaopa Uthenga Woipa? (Salimo 112:1-10)

  • 10:45 Phunziro Lachidule la Nsanja ya Olonda

  • 11:15 Nyimbo Na. 61 Komanso Kupuma

Masana

  • 12:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 12:45 Nyimbo Na. 122

  • 12:50 KUWERENGA BAIBULO MWASEWERO: “Nthawi Yodikira Yatha” (Chivumbulutso 10:6)

  • 1:20 Nyimbo Na. 126 Komanso Zilengezo

  • 1:30 Kodi Mwaphunzira Chiyani?

  • 1:40 N’chifukwa Chiyani Tikufunika ‘Kugwira Mwamphamvu Uthenga Wabwino’ Nanga Tingachite Bwanji Zimenezi? (1 Akorinto 2:16; 15:1, 2, 58; Maliko 6:30-34)

  • 2:30 Nyimbo Yatsopano Komanso Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena