Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w89 3/15 tsamba 25
  • Ripoti Lolongosoka la Mboni Yowona ndi Maso!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ripoti Lolongosoka la Mboni Yowona ndi Maso!
  • Nsanja ya Olonda—1989
  • Nkhani Yofanana
  • Kulambira Baala Nkhondo Yosatha M’mitima mwa Aisrayeli
    Nsanja ya Olonda—1999
  • Ugariti Mzinda Wakale Kumene Kunali Kuchimake Kolambira Baala
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Ino Ndi Nthawi Yofunika Kuchitapo Kanthu Mwachangu
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Kodi Mulungu Amavomereza Kulambira Kwamtundu Uliwonse?
    Nsanja ya Olonda—1996
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda—1989
w89 3/15 tsamba 25

Ripoti Lolongosoka la Mboni Yowona ndi Maso!

Lemba lofalitsidwa posachedwapa la chiUgaritic (KTU 1.161) likutsimikizira kudalirika kwa 2 Mafumu 10:19, 20. Kuti awononge alambiri a Baala, Mfumu Yehu analamula kuti: “Lalikirani msonkhano wopatulika wa Baala.” (Mulungu wonyenga, mothekera woimiridwa ndi kafano koumbidwa kulamanzere.) Mogwirizana ndi Vetus Testamentum, magazini yofalitsidwa mu Netherlands, kalongosoledweka kali “mKanani weniweni” ndipo kamatanthauza “ ‘zungulire wotsekedwa’: wakunja aliyense akanakhoza kulangidwa ndi temberero.” “Tsopano tikuzindikira kuti mkonzi wa ndimeyo mu 2 Mafumu mwachiwonekere akusonyeza chidziŵitso chabwino cha kugwiritsira ntchito mawu kwa chipembedzo kwa Chikanani,” yachitira ndemanga tero Vetus Testamentum.

[Mawu a Chithunzi patsamba 25]

Louvre Museum, Paris

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena