Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 April tsamba 2
  • Kusakhala Pabanja ndi Mphatso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kusakhala Pabanja ndi Mphatso
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Muzigwiritsa Ntchito Mwanzeru Nthawi Imene Simuli pa Banja
    Nsanja ya Olonda—2011
  • ‘Ilandireni’
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
  • Pamene Umbeta Uli Mphatso
    Galamukani!—1995
  • Umbeta—Njira Yopatsa Mphoto ya Moyo
    Nsanja ya Olonda—1987
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 April tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 AKORINTO 7-9

Kusakhala Pabanja ndi Mphatso

7:32, 35, 38

Kwa nthawi yaitali, Akhristu ambiri akhala akunena kuti kusakhala pabanja kumawapatsa mpata wochita zambiri potumikira Yehova. Amanenanso kuti kumawathandiza kuti adziwane ndi anthu ambiri komanso kuti azikonda kwambiri Yehova.

Abale atatu osakwatira ali paulendo wokalalikira ku Australia mu 1937; mlongo wosakwatiwa akufika ku Mexico mu 1947 kukachita utumiki waumishonale

mu 1937, abale ali paulendo wokalalikira ku Australia; mu 1947, mlongo amene anamaliza maphunziro a sukulu ya Giliyadi akufika ku Mexico

M’bale wosakwatira akulalikira ku Brazil; ophunzira omwe sali pabanja ali ku Sukulu ya Akhristu Olalikira za Ufumu ku Malawi

m’bale akulalikira ku Brazil; ali ku Sukulu ya Akhristu Olalikira za Ufumu ku Malawi

MAFUNSO OFUNIKA KUWAGANIZIRA: Ngati simuli pabanja, kodi mungatani kuti muzigwiritsa ntchito nthawi imeneyi mwanzeru?

Kodi abale ndi alongo mumpingo angathandize bwanji anthu amene sali pabanja?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena