Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 February tsamba 2
  • Pangano Lomwe Limakukhudzani

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pangano Lomwe Limakukhudzani
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova ndi Mulungu Wamapangano
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Pangano la Mulungu ndi “Bwenzi” Lake Likupindulitsa Kale Mamiliyoni Ambiri
    Chisungiko cha Padziko Lonse mu Ulamuliro wa “Kalonga wa Mtendere”
  • Mapangano Ophatikizapo Chifuno Chosatha cha Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1989
  • Madalitso Aakulu Kudzera m’Pangano Latsopano
    Nsanja ya Olonda—1998
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 February tsamba 2
Abulahamu akuyang’ana kumwamba.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 12-14

Pangano Lomwe Limakukhudzani

12:1-3; 13:14-17

  • Yehova anachita pangano ndi Abulahamu. Panganoli linathandiza kuti Yesu ndi odzozedwa akhale ovomerezeka mwalamulo kuti akalamulire ngati mafumu kumwamba

  • Panganoli linayamba kugwira ntchito m’chaka cha 1943 B.C.E., pamene Abulahamu anawoloka mtsinje wa Firate popita ku Kanani

  • Panganoli lipitirizabe kugwira ntchito kufikira pamene Ufumu wa Mesiya udzawononge adani onse a Mulungu n’kupereka madalitso kwa mabanja onse a padziko lapansi

Yehova anadalitsa Abulahamu chifukwa anali ndi chikhulupiriro cholimba. Kodi tikuyembekezera kudzalandira madalitso otani chifukwa cha pangano la Abulahamu?

Abulahamu ndi banja lake akudutsa mudzi wina m’Kanani.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena