Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsamba 5
  • Yehova Anapulumutsa Yosefe

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Anapulumutsa Yosefe
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Ndingachitirenji Choipa Chachikulu N’kuchimwira Mulungu?’
    Nsanja ya Olonda—2014
  • “Kodi Ine Ndatenga Malo a Mulungu?”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Yehova Amatithandiza Kuti Zinthu Zizitiyendera Bwino
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Ankasamalira Banja Lake Komanso Anakhalabe Wokhulupirika
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 May tsamba 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 40-41

Yehova Anapulumutsa Yosefe

41:9-13, 16, 29-32, 38-40

Yosefe anakhala kapolo komanso anakhala m’ndende kwa zaka pafupifupi 13 Yehova asanamupulumutse. M’malo mokwiya, Yosefe anaphunzira zinthu zambiri zabwino kuchokera pa zimene zinamuchitikira. (Sal. 105:17-19) Iye ankadziwa kuti Yehova sanamusiye. Kodi Yosefe anachita zinthu zabwino ziti ngakhale kuti ankakumana ndi mavuto?

  • Yosefe akupereka chakudya kwa akaidi anzake.

    Iye ankagwira ntchito mwakhama komanso anali wokhulupirika ndipo zimenezi zinachititsa kuti Yehova amudalitse.​—Gen. 39:21, 22

  • Yosefe akupereka chakudya kwa akaidi anzake.

    Iye ankachita zinthu mokoma mtima kwa ena ndipo sanabwezere anthu omwe anamuchitira nkhanza.—Gen. 40:5-7

Kodi zimene zinamuchitikira Yosefe zingandithandize bwanji kupirira mavuto anga?

Pamene ndikuyembekezera kuti Yehova adzandipulumutse pa Aramagedo, kodi ndi zinthu zabwino ziti zomwe ndingachite ngakhale kuti ndikukumana ndi mavuto?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena