Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 June tsamba 3
  • Chakudya pa Nthawi ya Njala

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chakudya pa Nthawi ya Njala
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Mapulogalamu a pa JW Broadcasting ‘Ndi Othandiza Komanso Olimbikitsa Kwambiri’
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2017
  • “Timakonda Kwambiri TV ya JW Broadcasting”
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2016
  • Kodi Tingagwiritse Ntchito Bwanji Zinthu Zimene Zinajambulidwa Kuti Tizimvetsera?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 June tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 46-47

Chakudya pa Nthawi ya Njala

47:13, 16, 19, 20, 23-25

Yosefe akugwira ntchito yoyang’anira chakudya ku Iguputo. Anthu ena akumubweretsera matumba a zakudya.

Masiku ano anthu ambiri akuvutika ndi njala yauzimu. (Amosi 8:11) Pogwiritsa ntchito Yesu Khristu, Yehova amatipatsa chakudya chambiri chauzimu chimene chimatithandiza.

  • Mabuku athu

  • Misonkhano ya mpingo

  • Misonkhano yadera ndi yachigawo

  • Zinthu zongomvetsera

  • Mavidiyo

  • JW.ORG

  • JW Broadcasting

Kodi ndikudzimana zinthu ziti kuti ndizidya patebulo la Yehova nthawi zonse?

M’bale akuchititsa Phunziro la ‘Nsanja ya Olonda.’ Abale ndi alongo ena akweza manja kuti apereke ndemanga.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena