Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 July tsamba 12
  • ‘Madalitso Onsewa . . . Adzakupeza’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Madalitso Onsewa . . . Adzakupeza’
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Musamaone Zinthu Zopanda Pake
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Yehova Anachita Pangano ndi Davide
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Zimene Yobu Anachita Kuti Akhalebe Woyera
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Zimene Tingaphunzire pa Mafanizo a mu Nyimbo Youziridwa
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 July tsamba 12
Banja la Chiisiraeli lakhala pansi pa mtengo pafupi ndi nyumba yawo ndipo likucheza mosangalala. Nkhosa zikudya chapafupi.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

’Madalitso Onsewa . . . Adzakupeza’

Anthu onse amene amamvera mawu a Yehova amalandira madalitso ambiri (De 28:1, 3-6; w10 12/15 19 ¶18)

Atumiki okhulupirika a Yehova adzapeza madalitso (De 28:2; w01 9/15 10 ¶2)

Yehova amafuna kuti tizichita zomwe amafuna ‘mokondwera, komanso ndi mtima wosangalala’ (De 28:45-47; w10 9/15 8 ¶4)

Abale ndi alongo a mitundu yosiyanasiyana akudya limodzi pambuyo pamsonkhano.

Atumiki a Yehova okhulupirika akusangalala ndi madalitso ambiri panopa, ndipo m’tsogolomu adzapeza madalitso enanso amene Yehova analonjeza.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena