Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 23:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Atafika anaona mfumu itaimirira pafupi ndi chipilala* pakhomo. Akalonga+ ndi anthu oimba malipenga anali limodzi ndi mfumuyo ndipo anthu onse amʼdzikolo ankasangalala+ komanso ankaimba malipenga. Panalinso oimba ndi zipangizo zoimbira amene ankatsogolera poimba nyimbo zotamanda. Ataliya ataona zimenezi anangʼamba zovala zake nʼkuyamba kukuwa kuti: “Mwandichitira chiwembu! Mwandichitira chiwembu!”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena