-
Ekisodo 34:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Poyankha Mulungu anati: “Tsopano ndichita nanu pangano ili: Ndidzachita zinthu zodabwitsa pamaso pa anthu ako onse, zinthu zimene sizinachitikepo padziko lonse lapansi kapena m’mitundu yonse.+ Ndipo anthu onse okuzungulirani adzaonadi ntchito za Yehova, chifukwa ndidzachita nanu chinthu chochititsa mantha.+
-