Salimo
Nyimbo Yokwerera Kumzinda. Salimo la Davide.
124 “Yehova akanapanda kukhala nafe,”+
Tsopano Isiraeli anene kuti,
2 “Yehova akanapanda kukhala nafe,+
Pamene anthu anatiukira,+
Pamene mkwiyo wawo unatiyakira.+
5 Madzi amphamvu akanatikokolola.
6 Yehova atamandike,
Chifukwa sanatipereke kwa iwo kuti atimbwandire ngati nyama.