Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 61
  • Mtundu wa Munthu Amene Muyenera Kukhala

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mtundu wa Munthu Amene Muyenera Kukhala
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Mtundu wa Munthu Amene Ndiyenera Kukhala
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Akutipempha Kuti: “Mwana Wanga Khala Wanzeru”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kutumikira Yehova Ndi Moyo Wonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Akutipempha Mokoma Mtima Kuti: “Mwana Wanga, Khala Wanzeru”
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 61

Nyimbo 61

Mtundu wa Munthu Amene Muyenera Kukhala

Losindikizidwa

(2 Petulo 3:11)

1. Ndithokoze bwanji, ndiperekenji

Kwa inu Yehova chifukwa cha moyo?

Mtima wangawu ndifuna ndiudziwe

Mawu anu Yehova andithandize.

Ndakulonjezani kukhala wanu.

Chifuniro chanu ndichita mwachangu

Ndasankhatu ndekha kutumikira,

Ndisangalatse inu Yehova.

2. Ndithandizenibe kudzifufuza

Ndikhaledi munthu amene mufuna.

Anthu otero mudzawasamalira

Kukhala mmodzi wa iwo ndakhumbira.

(Onaninso Sal. 18:25; 116:12; 119:37; Miy. 11:20.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena