Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsamba 5
  • Yehova Adzaweruza Aliyense Malinga ndi Ntchito Zake

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Adzaweruza Aliyense Malinga ndi Ntchito Zake
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Amapereka Mphoto kwa Onse Omwe Amamutumikira
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Kodi Mumasankha Anthu Otani Kuti Akhale Anzanu?
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
  • Zimene Zili M‘buku la Yeremiya
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Ebedi-meleki Ndi Chitsanzo Chabwino pa Nkhani ya Kulimba Mtima Komanso Kukoma Mtima
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 May tsamba 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YEREMIYA 39-43

Yehova Adzaweruza Aliyense Malinga ndi Ntchito Zake

Zedekiya sanamvere zimene Yehova anamuuza zoti akadzipereke yekha kwa mfumu ya Babulo

39:4-7

  • Ana a Zedekiya anaphedwa iye akuona ndipo kenako anamukolowola maso, anamumanga ndi maunyolo amkuwa n’kukamuika m’ndende ku Babulo mpaka anafera komweko

    Mfumu Zedekiya inalangidwa chifukwa chosamvera Yehova, inakolowoledwa maso ndiponso inamangidwa ndi maunyolo amkuwa

Ebedi-meleki anasonyeza kuti ankakhulupirira Yehova komanso ankadera nkhawa Yeremiya

39:15-18

  • Yehova analonjeza kuti adzapulumutsa Ebedi-meleki pamene Yuda azidzawonongedwa

    Ebedi-meleki analimba mtima kupita kwa Mfumu Zedekiya ndipo anapulumutsidwa pamene Yerusalemu ankawonongedwa

Yeremiya analalikira molimba mtima kwa zaka zambiri Yerusalemu asanawonongedwe

40:1-6

  • Yehova anateteza Yeremiya pamene mzinda wa Yerusalemu unazunguliridwa ndi adani ndipo anachititsa kuti Ababulo amumasule

    Yeremiya analalikira molimba mtima ndipo ankapatsidwa chakudya pa nthawi imene mzinda wa Yerusalemu unazunguliridwa ndi asilikali
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena