Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsamba 4
  • May 15-21

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • May 15-21
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 May tsamba 4

May 15-21

YEREMIYA 39-43

  • Nyimbo Na. 133 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • • “Yehova Adzaweruza Aliyense Malinga ndi Ntchito Zake”: (10 min.)

    • Yer. 39:4-7​—Zedekiya anakumana ndi mavuto chifukwa chosamvera Yehova (it-2-E 1228 ¶4)

    • Yer. 39:15-18​—Yehova anayamikira Ebedi-meleki chifukwa chomukhulupirira (w12 5/1 31 ¶5)

    • Yer. 40:1-6​—Yehova anasamalira Yeremiya yemwe anali mtumiki wake wokhulupirika (it-2-E 482)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Yer. 42:1-3; 43:2, 4​—Kodi tikuphunzira chiyani kuchokera pa zimene Yohanani analakwitsa? (w03 5/1 10 ¶10)

    • Yer. 43:6, 7​—Kodi zochitika zimene zafotokozedwa m’mavesiwa zili ndi ubwino wotani? (it-1-E 463 ¶4)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yer. 40:11–41:3

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Yes. 46:10​—Kuphunzitsa Choonadi. Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Chiv. 12:7-9, 12​—Kuphunzitsa Choonadi. Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bh 153 ¶19-20​—Muitanireni munthuyo kumisonkhano.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 90

  • “Yehova Sangaiwale Chikondi Chanu” (Sal. 71:18): (15 min.) Nkhani yokambirana. Poyamba, onetsani vidiyo yakuti Yehova Sangaiwale Chikondi Chanu.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia Mawu Omaliza ¶1-13

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 123 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena