Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 33
  • Umutulire Yehova Nkhawa Zako

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Umutulire Yehova Nkhawa Zako
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Umutulire Yehova Nkhawa Zako
    Imbirani Yehova
  • Umsenze Yehova Nkhaŵa Zako
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chikondi cha Mulungu Chokhulupirika
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Abusa Ndi Mphatso
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 33

NYIMBO 33

Umutulire Yehova Nkhawa Zako

Losindikizidwa

(Salimo 55)

  1. 1. Chonde ndimveni Yehova

    musandinyalanyaze.

    Ndikuvutika mumtima

    chonde mundithandize.

    (KOLASI)

    Tulira Yehova nkhawa,

    Iye sangakusiye wekha.

    Akuteteza chifukwa ndi

    wokhulupirika.

  2. 2. N’kanakhala ndi mapiko

    ndikanaulukatu,

    Kuti ndibisale

    kwa ondichitira zoipa.

    (KOLASI)

    Tulira Yehova nkhawa,

    Iye sangakusiye wekha.

    Akuteteza chifukwa ndi

    wokhulupirika.

  3. 3. M’lungu akatitonthoza

    timapeza mtendere.

    Amatithandiza kuti

    tipirire mavuto.

    (KOLASI)

    Tulira Yehova nkhawa,

    Iye sangakusiye wekha.

    Akuteteza chifukwa ndi

    wokhulupirika.

(Onaninso Sal. 22:5; 31:​1-24.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena