Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 122
  • Khalani Olimba Komanso Osasunthika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani Olimba Komanso Osasunthika
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Olimba, Osasunthika
    Imbirani Yehova
  • Khalani Okhazikika, Osasunthika!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Khalani Olimba, Osasunthika”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Adzakulimbitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 122

NYIMBO 122

Khalani Olimba Komanso Osasunthika

Losindikizidwa

(1  Akorinto 15:58)

  1. 1. Anthu akuvutika kwambiri

    Ndipo akuopa zam’tsogolo.

    Ife tilimbe tisasunthike

    Potumikira M’lungu.

    (KOLASI)

    Tiyenera kulimba.

    Tisiyane ndi dziko.

    Tikhale olimba.

    Tidzapeza moyo.

  2. 2. Misampha ndi yambiri m’dzikoli

    Koma tingaipewe mwanzeru.

    Tikamadanatu ndi zoipa

    Sitidzasunthikadi.

    (KOLASI)

    Tiyenera kulimba.

    Tisiyane ndi dziko.

    Tikhale olimba.

    Tidzapeza moyo.

  3. 3. Tizilambira Yehova yekha.

    Tim’tumikire ndi mtima wonse.

    Tizilalikiradi mwakhama.

    Mapeto akubwera.

    (KOLASI)

    Tiyenera kulimba.

    Tisiyane ndi dziko.

    Tikhale olimba.

    Tidzapeza moyo.

(Onaninso Luka 21:9; 1 Pet. 4:7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena