Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/15 tsamba 8
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Zomwe Munganene Pogaŵira Magazini
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2004
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Zomwe Munganene Pogawira Magazini
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2008
  • Zomwe Munganene Pogawira Magazini
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2006
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 6/15 tsamba 8

Zitsanzo za Ulaliki

Nsanja ya Olonda July 1

“Anthufe timakumana ndi zinthu zambiri zodetsa nkhawa pa moyo wathu. Kodi mukuganiza kuti zimene Yesu ananena palemba ili ndi zothandiza masiku ano? [Werengani Mateyu 6:25 kenako yembekezerani kuti ayankhe.] Nsanja ya Olonda iyi ikufotokoza mmene mfundo za m’Baibulo zingatithandizire kuchepetsa nkhawa zimene zimayamba chifukwa chosowa ndalama, mavuto a m’banja komanso zinthu zina zoopsa.”

Galamukani! July

“Masiku ano anthu ambiri amada nkhawa chifukwa cha mavuto amene akukumana nawo. Kodi inunso mumaona choncho? [Yembekezerani ayankhe.] Baibulo limanena kuti zimene timachita tikakumana ndi mavuto zikhoza kutithandiza kupirira kapena ayi. [Werengani Miyambo 24:10.] Magazini iyi ili ndi malangizo amene angatithandize ngati titakumana ndi mavuto aakulu. Komanso ikufotokoza zimene anthu ena akuchita kuti apirire mavuto amene akukumana nawo.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena