LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
Baibo ya Cimasulilo ca Dziko Latsopano

Za m’Buku la Luka

LUKA

ZA M’BUKULI

  • 1

    • Kalata yopita kwa Teofilo (1-4)

    • Mngelo Gabirieli anenelatu za kubadwa kwa Yohane M’batizi (5-25)

    • Mngelo Gabirieli anenelatu za kubadwa kwa Yesu (26-38)

    • Mariya apita kwa Elizabeti (39-45)

    • Mariya alemekeza Yehova (46-56)

    • Kubadwa kwa Yohane ndi mmene anamupatsila dzina (57-66)

    • Ulosi wa Zekariya (67-80)

  • 2

    • Kubadwa kwa Yesu (1-7)

    • Angelo aonekela kwa abusa (8-20)

    • Mdulidwe ndi kuyeletsedwa (21-24)

    • Simiyoni aona Khristu (25-35)

    • Anna akamba zokhudza mwanayo (36-38)

    • Abwelela ku Nazareti (39, 40)

    • Yesu wa zaka 12 apita ku kacisi (41-52)

  • 3

    • Ciyambi ca nchito ya Yohane (1, 2)

    • Yohane alalikila za ubatizo (3-20)

    • Ubatizo wa Yesu (21, 22)

    • Mzele wa makolo a Yesu Khristu (23-38)

  • 4

    • Mdyelekezi ayesa Yesu (1-13)

    • Yesu ayamba kulalikila ku Galileya (14, 15)

    • Yesu akanidwa ku Nazareti (16-30)

    • Zimene zinacitika m’sunagoge ku Kaperenao (31-37)

    • Apongozi aakazi a Simoni ndi anthu ena acilitsidwa (38-41)

    • Khamu la anthu lipeza Yesu ku malo opanda anthu (42-44)

  • 5

    • Akupha nsomba mozizwitsa; ophunzila oyambilila (1-11)

    • Wakhate acilitsidwa (12-16)

    • Yesu acilitsa munthu wofa ziwalo (17-26)

    • Yesu aitana Levi (27-32)

    • Funso pa nkhani ya kusala kudya (33-39)

  • 6

    • Yesu, “Mbuye wa Sabata” (1-5)

    • Munthu wopuwala dzanja acilitsidwa (6-11)

    • Atumwi 12 (12-16)

    • Yesu aphunzitsa ndi kucilitsa (17-19)

    • Anthu acimwemwe komanso anthu atsoka (20-26)

    • Kukonda adani (27-36)

    • Lekani kuweluza ena (37-42)

    • Umadziwika ndi zipatso zake (43-45)

    • Nyumba yomangidwa bwino; nyumba yopanda maziko (46-49)

  • 7

    • Cikhulupililo ca kapitawo wa asilikali (1-10)

    • Yesu acilitsa mwana wamwamuna wa mkazi wamasiye ku Naini (11-17)

    • Yohane M’batizi atamandidwa (18-30)

    • Adzudzula m’badwo wosamvela (31-35)

    • Mayi wocimwa akhululukidwa (36-50)

      • Fanizo la anthu amene anatenga nkhongole (41-43)

  • 8

    • Azimayi amene anali kutsatila Yesu (1-3)

    • Fanizo la wofesa mbewu (4-8)

    • Cifukwa cake Yesu anagwilitsa nchito mafanizo (9, 10)

    • Afotokoza tanthauzo la fanizo la wofesa mbewu (11-15)

    • Nyale saibwinikila (16-18)

    • Amayi ake a Yesu ndi abale ake (19-21)

    • Yesu aleketsa namondwe (22-25)

    • Yesu atumiza ziwanda m’nkhumba (26-39)

    • Mwana wamkazi wa Yairo; mzimayi agwila covala cakunja ca Yesu (40-56)

  • 9

    • Alangiza atumwi 12 molalikilila (1-6)

    • Herode adabwa naye kwambili Yesu (7-9)

    • Yesu adyetsa anthu 5,000 (10-17)

    • Petulo azindikila kuti Yesu ndi Khristu (18-20)

    • Yesu anenelatu za imfa yake (21, 22)

    • Zimene ophunzila oona a Yesu amacita (23-27)

    • Kusandulika kwa Yesu (28-36)

    • Kamnyamata kogwidwa ndi ciwanda kacilitsidwa (37-43a)

    • Kaciwili, Yesu anenelatu za imfa yake (43b-45)

    • Ophunzila akangana zakuti wamkulu ndani (46-48)

    • Aliyense amene satsutsana nafe ali ku mbali yathu (49, 50)

    • Mudzi wina wa Asamariya ukana Yesu (51-56)

    • Mmene tingatsatilile Yesu (57-62)

  • 10

    • Yesu atuma ophunzila 70 (1-12)

    • Tsoka ku mizinda yosalapa (13-16)

    • Ophunzila 70 abwelako (17-20)

    • Yesu atamanda Atate ake cifukwa cokonda anthu odzicepetsa (21-24)

    • Fanizo la Msamariya wacifundo (25-37)

    • Yesu apita kwa Marita ndi Mariya (38-42)

  • 11

    • Mmene tingapemphelele (1-13)

      • Pemphelo la citsanzo (2-4)

    • Ziwanda zitulutsidwa ndi cala ca Mulungu (14-23)

    • Mzimu wonyansa ubwelelanso (24-26)

    • Cimwemwe ceniceni (27, 28)

    • Cizindikilo ca Yona (29-32)

    • Nyale ya thupi (33-36)

    • Tsoka kwa atsogoleli onyenga acipembedzo (37-54)

  • 12

    • Zofufumitsa za Afarisi (1-3)

    • Opani Mulungu, osati anthu (4-7)

    • Kuvomeleza kuti ndife ophunzila a Khristu (8-12)

    • Fanizo la munthu wacuma wopusa (13-21)

    • Lekani kuda nkhawa (22-34)

      • Kagulu ka nkhosa (32)

    • Kukhala maso (35-40)

    • Woyang’anila wokhulupilika komanso woyang’anila wosakhulupilika (41-48)

    • Osati mtendele, koma magawano (49-53)

    • Kufunika kodziwa tanthauzo la zimene zikucitika (54-56)

    • Kuthetsa mikangano (57-59)

  • 13

    • Lapani, apo ayi muwonongedwa (1-5)

    • Fanizo la mtengo wamkuyu wosabala zipatso (6-9)

    • Mzimayi wopindika msana acilitsidwa pa Sabata (10-17)

    • Fanizo la kanjele ka mpilu komanso la zofufumitsa (18-21)

    • Khama n’lofunika kuti tilowe pa khomo lopanikiza (22-30)

    • Herode achulidwa kuti “nkhandwe” (31-33)

    • Yesu adandaula za Yerusalemu (34, 35)

  • 14

    • Mwamuna wina wodwala matenda otupikana acilitsidwa pa Sabata (1-6)

    • Khalani mlendo wodzicepetsa (7-11)

    • Muziitana anthu amene sangakubwezeleni (12-14)

    • Fanizo la anthu amene anakana kupita ku phwando (15-24)

    • Zofunika kucita kuti munthu akhale wophunzila (25-33)

    • Mcele umene watha mphamvu (34, 35)

  • 15

    • Fanizo la nkhosa yosecela (1-7)

    • Fanizo la khobili lotayika (8-10)

    • Fanizo la mwana wolowelela (11-32)

  • 16

    • Fanizo la woyang’anila nyumba wosalungama (1-13)

      • ‘Munthu wokhulupilika pa cinthu cacing’ono amakhalanso wokhulupilika pa cacikulu (10)

    • Cilamulo komanso Ufumu wa Mulungu (14-18)

    • Fanizo la munthu wolemela ndi Lazaro (19-31)

  • 17

    • Kupunthwa, kukhululukila, ndi cikhulupililo (1-6)

    • Akapolo opanda pake (7-10)

    • Anthu 10 akhate acilitsidwa (11-19)

    • Kubwela kwa Ufumu wa Mulungu (20-37)

      • Ufumu wa Mulungu “uli pakati panu” (21)

      • “Kumbukilani mkazi wa Loti” (32)

  • 18

    • Fanizo la mkazi wamasiye wolimbikila (1-8)

    • Mfarisi ndi wokhometsa misonkho (9-14)

    • Yesu ndi ana aang’ono (15-17)

    • Funso la wolamulila wacuma (18-30)

    • Yesu anenelatunso za imfa yake (31-34)

    • Munthu wakhungu wopemphapempha ayamba kuona (35-43)

  • 19

    • Yesu apita kwa Zakeyo (1-10)

    • Fanizo la ndalama 10 za mina (11-27)

    • Yesu atamandidwa polowa mu Yerusalemu (28-40)

    • Yesu alilila Yerusalemu (41-44)

    • Yesu ayeletsa kacisi (45-48)

  • 20

    • Anthu akayikila mphamvu za Yesu (1-8)

    • Fanizo la alimi akupha (9-19)

    • Mulungu ndi Kaisara (20-26)

    • Funso pa nkhani ya kuuka kwa akufa (27-40)

    • Kodi Khristu ndi mwana wa Davide? (41-44)

    • Acenjeza anthu kuti asamale ndi alembi (45-47)

  • 21

    • Tumakobili tuwili twa mkazi wamasiye wosauka (1-4)

    • CIZINDIKILO CA ZIMENE ZIKUBWELA (5-36)

      • Nkhondo, zivomezi zamphamvu, milili, ndi njala (10, 11)

      • Yerusalemu adzazungulilidwa ndi magulu a asilikali (20)

      • Nthawi zoikika za anthu a mitundu (24)

      • Kubwela kwa Mwana wa Munthu (27)

      • Fanizo la mtengo wamkuyu (29-33)

      • Khalanibe maso (34-36)

    • Yesu aphunzitsa m’kacisi (37, 38)

  • 22

    • Ansembe akonza ciwembu ca kupha Yesu (1-6)

    • Kukonzekela Pasika wothela (7-13)

    • Kukhazikitsidwa kwa Mgonelo wa Ambuye (14-20)

    • “Wondipeleka uja ali nane pathebulo pano” (21-23)

    • Akangana kwambili zakuti wamkulu ndani (24-27)

    • Cipangano ca Yesu ca Ufumu (28-30)

    • Yesu akambilatu zakuti Petulo adzamukana (31-34)

    • Kufunika kokhala okonzeka; malupanga awili (35-38)

    • Pemphelo la Yesu pa Phili la Maolivi (39-46)

    • Yesu agwidwa (47-53)

    • Petulo akana Yesu (54-62)

    • Yesu acitidwa zacipongwe (63-65)

    • Azengedwa mlandu ku Khoti Yaikulu ya Ayuda (66-71)

  • 23

    • Yesu aonekela pamaso pa Pilato ndi Herode (1-25)

    • Yesu ndi zigawenga ziwili apacikidwa pa mitengo (26-43)

      • “Iwe udzakhala ndi ine m’Paradaiso” (43)

    • Imfa ya Yesu (44-49)

    • Yesu aikidwa m’manda (50-56)

  • 24

    • Yesu aukitsidwa (1-12)

    • Pa msewu wopita ku Emau (13-35)

    • Yesu aonekela kwa ophunzila (36-49)

    • Yesu akwela kumwamba (50-53)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani