LUKA
ZA M’BUKULI
-
Kalata yopita kwa Teofilo (1-4)
Mngelo Gabirieli anenelatu za kubadwa kwa Yohane M’batizi (5-25)
Mngelo Gabirieli anenelatu za kubadwa kwa Yesu (26-38)
Mariya apita kwa Elizabeti (39-45)
Mariya alemekeza Yehova (46-56)
Kubadwa kwa Yohane ndi mmene anamupatsila dzina (57-66)
Ulosi wa Zekariya (67-80)
-
Yesu, “Mbuye wa Sabata” (1-5)
Munthu wopuwala dzanja acilitsidwa (6-11)
Atumwi 12 (12-16)
Yesu aphunzitsa ndi kucilitsa (17-19)
Anthu acimwemwe komanso anthu atsoka (20-26)
Kukonda adani (27-36)
Lekani kuweluza ena (37-42)
Umadziwika ndi zipatso zake (43-45)
Nyumba yomangidwa bwino; nyumba yopanda maziko (46-49)
-
Azimayi amene anali kutsatila Yesu (1-3)
Fanizo la wofesa mbewu (4-8)
Cifukwa cake Yesu anagwilitsa nchito mafanizo (9, 10)
Afotokoza tanthauzo la fanizo la wofesa mbewu (11-15)
Nyale saibwinikila (16-18)
Amayi ake a Yesu ndi abale ake (19-21)
Yesu aleketsa namondwe (22-25)
Yesu atumiza ziwanda m’nkhumba (26-39)
Mwana wamkazi wa Yairo; mzimayi agwila covala cakunja ca Yesu (40-56)
-
Alangiza atumwi 12 molalikilila (1-6)
Herode adabwa naye kwambili Yesu (7-9)
Yesu adyetsa anthu 5,000 (10-17)
Petulo azindikila kuti Yesu ndi Khristu (18-20)
Yesu anenelatu za imfa yake (21, 22)
Zimene ophunzila oona a Yesu amacita (23-27)
Kusandulika kwa Yesu (28-36)
Kamnyamata kogwidwa ndi ciwanda kacilitsidwa (37-43a)
Kaciwili, Yesu anenelatu za imfa yake (43b-45)
Ophunzila akangana zakuti wamkulu ndani (46-48)
Aliyense amene satsutsana nafe ali ku mbali yathu (49, 50)
Mudzi wina wa Asamariya ukana Yesu (51-56)
Mmene tingatsatilile Yesu (57-62)
-
Zofufumitsa za Afarisi (1-3)
Opani Mulungu, osati anthu (4-7)
Kuvomeleza kuti ndife ophunzila a Khristu (8-12)
Fanizo la munthu wacuma wopusa (13-21)
Lekani kuda nkhawa (22-34)
Kagulu ka nkhosa (32)
Kukhala maso (35-40)
Woyang’anila wokhulupilika komanso woyang’anila wosakhulupilika (41-48)
Osati mtendele, koma magawano (49-53)
Kufunika kodziwa tanthauzo la zimene zikucitika (54-56)
Kuthetsa mikangano (57-59)
-
Lapani, apo ayi muwonongedwa (1-5)
Fanizo la mtengo wamkuyu wosabala zipatso (6-9)
Mzimayi wopindika msana acilitsidwa pa Sabata (10-17)
Fanizo la kanjele ka mpilu komanso la zofufumitsa (18-21)
Khama n’lofunika kuti tilowe pa khomo lopanikiza (22-30)
Herode achulidwa kuti “nkhandwe” (31-33)
Yesu adandaula za Yerusalemu (34, 35)
-
Ansembe akonza ciwembu ca kupha Yesu (1-6)
Kukonzekela Pasika wothela (7-13)
Kukhazikitsidwa kwa Mgonelo wa Ambuye (14-20)
“Wondipeleka uja ali nane pathebulo pano” (21-23)
Akangana kwambili zakuti wamkulu ndani (24-27)
Cipangano ca Yesu ca Ufumu (28-30)
Yesu akambilatu zakuti Petulo adzamukana (31-34)
Kufunika kokhala okonzeka; malupanga awili (35-38)
Pemphelo la Yesu pa Phili la Maolivi (39-46)
Yesu agwidwa (47-53)
Petulo akana Yesu (54-62)
Yesu acitidwa zacipongwe (63-65)
Azengedwa mlandu ku Khoti Yaikulu ya Ayuda (66-71)