LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w14 10/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
w14 10/15 masa. 1-2

Zamkati

October 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

DECEMBER 1-7, 2014

Khalani ndi Cikhulupililo Cosagwedela mu Ufumu

TSAMBA 7 • NYIMBO: 108, 129

DECEMBER 8-14, 2014

Mudzakhala “Ufumu wa Ansembe”

TSAMBA 13 • NYIMBO: 98, 102

DECEMBER 15-21, 2014

Muziyamikila Mwai Wanu Wogwila Nchito ndi Yehova

TSAMBA 23 • NYIMBO: 120, 44

DECEMBER 22-28, 2014

“Ikani Maganizo Anu pa Zinthu Zakumwamba”

TSAMBA 28 • NYIMBO: 70, 57

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ Khalani ndi Cikhulupililo Cosagwedela mu Ufumu

▪ Mudzakhala “Ufumu wa Ansembe”

Ufumu wa Mesiya ndiwo njila yokha imene Yehova adzagwilitsila nchito kuti akwanilitse cifunilo cake ca dziko lapansi ndi ca anthu. Pamene tikambilana mapangano angapo ochulidwa m’Baibulo, tidzaphunzila mmene amagwilizanilana ndi boma lakumwamba. Tidzaphunzila cifukwa cake tiyenela kukhala ndi cidalilo colimba mu Ufumu.

▪ Muziyamikila Mwai Wanu Wogwila Nchito ndi Yehova

M’nkhani ino, tidzaphunzila zitsanzo zakale ndi zamakono za anthu amene atumikila Yehova. Idzatithandiza kuyamikila mwai wathu wogwila nchito ndi Mulungu, umene tiyenela kuyamikila kwambili.

▪ “Ikani Maganizo Anu pa Zinthu Zakumwamba”

M’masiku ano otsiliza, timakumana ndi zinthu zambili zimene zimayesa cikhulupililo cathu. Nanga tingaphunzile ciani kwa anthu akale monga Abulahamu ndi Mose, amene anakumana ndi mayeselo ofanana ndi athu? Nkhani ino idzatithandiza kupilila ndi kutilimbikitsa kuika maganizo athu pa Mulungu ndi Ufumu wake.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

3 Anadzipeleka Mofunitsitsa—ku Taiwan

18 Cocitika Cosaiŵalika pa Utumiki Wanga wa Ufumu

CIKUTO: Alongo aŵili alalikila kwa anthu amene akuyenda mumseu waukulu pafupi ndi mapili a Mbololo, kum’mawa koma cakum’mwela pang’ono m’tauni ya Tausa, ku Taita

KU KENYA

KULI ANTHU

44,250,000

OFALITSA

26,060

MAPHUNZILO A BAIBULO

43,034

OPEZEKA PA CIKUMBUTSO MU 2013

60,166

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani